Mateyu 1:11 - Buku Lopatulika11 ndi Yosiya anabala Yekoniya ndi abale ake pa nthawi yakutengedwa kunka ku Babiloni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 ndi Yosiya anabala Yekoniya ndi abale ake pa nthawi yakutengedwa kunka ku Babiloni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Yosiya adabereka Yekoniya ndi abale ake, pa nthaŵi imene Aisraele adaatengedwa ukapolo kupita ku Babiloni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Yosiya anali atabala Yekoniya ndi abale ake pamene Ayuda anatengedwa ukapolo kupita ku Babuloni. Onani mutuwo |