Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 1:10 - Buku Lopatulika

10 ndi Hezekiya anabala Manase; ndi Manase anabala Amoni; ndi Amoni anabala Yosiya;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 ndi Hezekiya anabala Manase; ndi Manase anabala Amoni; ndi Amoni anabala Yosiya;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Hezekiya adabereka Manase, Manase adabereka Amoni, Amoni adabereka Yosiya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Hezekiya anabereka Manase, Manase anabereka Amoni, Amoni anabereka Yosiya.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 1:10
8 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anafuula mwa mau a Yehova kutemberera guwa la nsembe, nati, Guwa la nsembe, guwa la nsembe, atero Yehova, Taona mwana adzabadwa m'nyumba ya Davide, dzina lake ndi Yosiya, adzaphera pa iwe ngati nsembe anthu ansembe a misanje, amene alikufukiza zonunkhira pa iwe, nadzatentha pa iwe mafupa a anthu.


Nagona Hezekiya ndi makolo ake; nakhala mfumu m'malo mwake Manase mwana wake.


Ndipo Hezekiya anagona ndi makolo ake, namuika polowerera kumanda a ana a Davide; ndi Ayuda onse ndi okhala mu Yerusalemu anamchitira ulemu pa imfa yake. Ndipo Manase mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake.


ndi Yosiya anabala Yekoniya ndi abale ake pa nthawi yakutengedwa kunka ku Babiloni.


ndi Uziya anabala Yotamu; ndi Yotamu anabala Ahazi; ndi Ahazi anabala Hezekiya;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa