Masalimo 99:6 - Buku Lopatulika6 Mwa ansembe ake muli Mose ndi Aroni, ndi Samuele mwa iwo akuitanira dzina lake; anaitana kwa Yehova, ndipo Iye anawayankha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Mwa ansembe ake muli Mose ndi Aroni, ndi Samuele mwa iwo akuitanira dzina lake; anaitana kwa Yehova, ndipo Iye anawayankha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Mose ndi aroni anali ena mwa ansembe ake, Samuele nayenso anali mmodzi mwa anthu otama dzina la Chauta mopemba. Ankalira kwa Chauta Iye nkumaŵayankha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mose ndi Aaroni anali ena mwa ansembe ake, Samueli anali pamodzi ndi iwo amene anayitana pa dzina lake; iwo anayitana Yehova ndipo Iyeyo anawayankha. Onani mutuwo |