Masalimo 94:6 - Buku Lopatulika6 Amapha wamasiye ndi mlendo, nawapha ana amasiye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Amapha wamasiye ndi mlendo, nawapha ana amasiye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Amapha akazi amasiye ndi alendo okhala nawo m'dziko mwao, amaphanso ana amasiye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Amaphanso amayi a masiye ndi alendo okhala nawo mʼdziko; amapha ana amasiye. Onani mutuwo |