Masalimo 94:11 - Buku Lopatulika11 Yehova adziwa zolingalira za munthu, kuti zili zachabe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Yehova adziwa zolingalira za munthu, kuti zili zachabe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Chauta amadziŵa maganizo a anthu kuti ndi mpweya chabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Yehova amadziwa maganizo a munthu; Iye amadziwa kuti maganizowo ndi achabechabe. Onani mutuwo |