Masalimo 94:10 - Buku Lopatulika10 Kodi Iye wakulangiza mitundu ya anthu, ndiye wosadzudzula? Si ndiye amene aphunzitsa munthu nzeru? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Kodi Iye wakulangiza mitundu ya anthu, ndiye wosadzudzula? Si ndiye amene aphunzitsa munthu nzeru? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Kodi wolangiza mitundu ya anthu, sangathe kulanga? Kodi wophunzitsa anthu onse, alibe nzeru? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kodi Iye amene amalangiza mitundu ya anthu sangathenso kulanga? Kodi Iye amene amaphunzitsa munthu angasowe nzeru? Onani mutuwo |