Masalimo 92:15 - Buku Lopatulika15 kulalikira kuti Yehova ngwolunjika; Iye ndiye thanthwe langa, ndipo mwa Iye mulibe chosalungama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 kulalikira kuti Yehova ngwolunjika; Iye ndiye thanthwe langa, ndipo mwa Iye mulibe chosalungama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 imaonetsa kuti Chauta ndi wolungama. Iye ndiye thanthwe langa mwa Iye mulibe chokhota. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 kulengeza kuti, “Yehova ndi wolungama; Iye ndiye Thanthwe langa, ndipo mwa Iye mulibe choyipa.” Onani mutuwo |