Masalimo 9:5 - Buku Lopatulika5 Mwadzudzula amitundu, mwaononga woipayo, mwafafaniza dzina lao kunthawi yonka muyaya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mwadzudzula amitundu, mwaononga woipayo, mwafafaniza dzina lao kunthawi yonka muyaya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mwaimba mlandu mafuko a anthu, mwaononga anthu oipa. Adzaiŵalika mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mwadzudzula mitundu ya anthu ndipo mwawononga anthu oyipa; Inu mwafafaniza dzina lawo kwamuyaya. Onani mutuwo |
Ndipo pamene Davide anamva kuti Nabala adamwalira, iye anati, Alemekezedwe Yehova, amene anaweruza mlandu wa mtonzo wanga wochokera ku dzanja la Nabala, naletsa mnyamata wake pa choipa; ndipo Yehova anabwezera pamutu pa Nabala choipa chake. Ndipo Davide anatumiza wokamfunsira Abigaile, zakuti amtengere akhale mkazi wake.