Masalimo 86:12 - Buku Lopatulika12 Ndidzakuyamikani, Ambuye, Mulungu wanga, ndi mtima wanga wonse; ndipo ndidzalemekeza dzina lanu nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndidzakuyamikani, Ambuye, Mulungu wanga, ndi mtima wanga wonse; ndipo ndidzalemekeza dzina lanu nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Inu Ambuye, Mulungu wanga, ndikukuthokozani ndi mtima wanga wonse, ndidzalemekeza ukulu wanu mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ndidzakutamandani Ambuye Mulungu wanga, ndi mtima wanga wonse; ndidzalemekeza dzina lanu kwamuyaya. Onani mutuwo |