Masalimo 86:13 - Buku Lopatulika13 Pakuti chifundo chanu cha pa ine nchachikulu; ndipo munalanditsa moyo wanga kunsi kwa manda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pakuti chifundo chanu cha pa ine nchachikulu; ndipo munalanditsa moyo wanga kunsi kwa manda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Paja chikondi chanu chosasinthika kwa ine nchachikulu, Mwandipulumutsa ku malo akuya a anthu akufa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu kwa ine; mwandipulumutsa ku malo ozama a manda. Onani mutuwo |