Masalimo 86:11 - Buku Lopatulika11 Mundionetse njira yanu, Yehova; ndidzayenda m'choonadi chanu, muumbe mtima wanga ukhale umodzi kuti uliope dzina lanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Mundionetse njira yanu, Yehova; ndidzayenda m'choonadi chanu, muumbe mtima wanga ukhale umodzi kuti uliope dzina lanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Phunzitseni njira zanu, Inu Chauta, kuti ndiziyenda m'zoona zanu. Mundipatse mtima wosagaŵikana, kuti ndiziwopa dzina lanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndiphunzitseni njira yanu Yehova, ndipo ndidzayenda mʼchoonadi chanu; patseni mtima wosagawikana kuti ndilemekeze dzina lanu. Onani mutuwo |