Masalimo 86:10 - Buku Lopatulika10 Pakuti Inu ndinu wamkulu, ndi wakuchita zodabwitsa; Inu ndinu Mulungu, nokhanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pakuti Inu ndinu wamkulu, ndi wakuchita zodabwitsa; Inu ndinu Mulungu, nokhanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Pakuti Inu ndinu wamkulu, mumachita zinthu zodabwitsa, Inu nokha ndinu Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Pakuti ndinu wamkulu ndipo mumachita zodabwitsa; Inu nokha ndiye Mulungu. Onani mutuwo |