Masalimo 84:4 - Buku Lopatulika4 Odala iwo akugonera m'nyumba mwanu; akulemekezani chilemekezere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Odala iwo akugonera m'nyumba mwanu; akulemekezani chilemekezere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ngodala anthu amene amakhala m'Nyumba mwanu, namaimba nyimbo zotamanda Inu nthaŵi zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Odala amene amakhala mʼNyumba yanu; nthawi zonse amakutamandani. Sela Onani mutuwo |