Masalimo 84:5 - Buku Lopatulika5 Wodala munthu amene mphamvu yake ili mwa Inu; mumtima mwake muli makwalala a ku Ziyoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Wodala munthu amene mphamvu yake ili mwa Inu; mumtima mwake muli makwalala a ku Ziyoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ngodala anthu amene mphamvu zao nzochokera kwa Inu, amene m'mitima mwao amafunitsitsa kudzera m'miseu yopita ku Ziyoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Odala amene mphamvu yawo ili mwa Inu, mitima yawo ikufunitsitsa kuyenda mʼmisewu yopita ku Ziyoni. Onani mutuwo |