Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 84:2 - Buku Lopatulika

2 Moyo wanga ulakalaka, inde ukomokanso ndi kufuna mabwalo a Yehova; mtima wanga ndi thupi langa zifuulira kwa Mulungu wamoyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Moyo wanga ulakalaka, inde ukomokanso ndi kufuna mabwalo a Yehova; mtima wanga ndi thupi langa zifuulira kwa Mulungu wamoyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Mtima wanga ukulakalaka, mpaka kukomoka, kufunitsitsa kuwona mabwalo a Chauta. Inu Mulungu wamoyo, ndikukuimbirani mwachimwemwe ndi mtima wanga wonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Moyo wanga ukulakalaka, mpaka kukomoka, kufuna mabwalo a Yehova; Mtima wanga ndi thupi langa zikufuwulira Mulungu wamoyo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 84:2
12 Mawu Ofanana  

Ha! Ndikadadziwa kumene ndikampeza Mulungu, kuti ndifike kumpando wake!


Mtima wanga wasweka ndi kukhumba maweruzo anu nyengo zonse.


Moyo wanga unakomoka ndi kukhumba chipulumutso chanu: Ndinayembekezera mau anu.


Nditambalitsira manja anga kwa Inu: Moyo wanga ulira Inu monga dziko lolira mvula.


Likatha thupi langa ndi mtima wanga, Mulungu ndiye thanthwe la mtima wanga, ndi cholandira changa chosatha.


Ndikulumbirirani, ana aakazi inu a ku Yerusalemu, mukapeza bwenzi langa, mudzamuuza chiyani? Kuti ndadwala ndi chikondi.


Ndi moyo wanga ndinakhumba Inu usiku; inde ndi mzimu wanga wa mwa ine ndidzafuna Inu mwakhama; pakuti pamene maweruziro anu ali padziko lapansi, okhala m'dziko lapansi adzaphunzira chilungamo.


Mwenzi mutang'amba kumwamba ndi kutsikira pansi, kuti mapiri agwedezeke pamaso panu;


Ha? Mahema ako ngokoma, Yakobo; zokhalamo zako, Israele!


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa