Masalimo 81:9 - Buku Lopatulika9 Kwanu kusakhale mulungu wofuma kwina; nusagwadire mulungu wachilendo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Kwanu kusakhale mulungu wofuma kwina; nusagwadire mulungu wachilendo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Pasadzakhale mulungu wachilendo pakati panu. Musadzapembedze mulungu wina ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Musadzakhale ndi mulungu wachilendo pakati panu; musadzagwadire mulungu wina. Onani mutuwo |