Masalimo 81:5 - Buku Lopatulika5 Anachiika chikhale mboni kwa Yosefe, pakutuluka iye kudziko la Ejipito. Komwe ndinamva chinenedwe chosadziwa ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Anachiika chikhale mboni kwa Yosefe, pakutuluka iye kudziko la Ejipito. Komwe ndinamva chinenedwe chosadziwa ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Adalipereka lamulolo kwa zidzukulu za Yosefe pamene zinkatuluka m'dziko la Ejipito. Ndikumva liwu limene sindidalimve ndi kale lonse, lakuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Iye anapereka lamulolo kwa zidzukulu za Yosefe pamene anatuluka kulimbana ndi Igupto, kumene tinamva chiyankhulo chimene sitinachidziwe. Onani mutuwo |