Masalimo 80:14 - Buku Lopatulika14 Bwererani, tikupemphani, Mulungu wa makamu; suzumirani muli m'mwamba, nimupenye, ndi kuzonda mpesa uwu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Bwererani, tikupemphani, Mulungu wa makamu; suzumirani muli m'mwamba, nimupenye, ndi kuzonda mpesa uwu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Mutembenukirenso kwa ife, Inu Mulungu Wamphamvuzonse, muyang'ane Inu okhala kumwamba, ndipo muwone. Samalani mpesawo, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Bweraninso kwa ife Inu Mulungu Wamphamvuzonse! Yangʼanani pansi muli kumwambako ndipo muone! Uyangʼanireni mpesa umenewu, Onani mutuwo |