Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 80:11 - Buku Lopatulika

11 Unatambalitsa mphanda zake mpaka kunyanja, ndi mitsitsi yake kufikira ku Mtsinje.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Unatambalitsa mphanda zake mpaka kunyanja, ndi mitsitsi yake kufikira ku Mtsinje.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Nthambizo zidafika mpaka ku nyanja yaikulu yakuzambwe, ndipo mphukira zake mpaka ku mtsinje waukulu wakuvuma.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Unatambalitsa nthambi zake mpaka ku nyanja, mphukira zake mpaka ku mtsinje.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 80:11
6 Mawu Ofanana  

Tsiku lomwelo Yehova anapangana chipangano ndi Abramu, nati, Ndidzapatsa mbeu zako dziko ili, kuyambira pamtsinje wa ku Ejipito kufikira pamtsinje waukulu, mtsinje wa Yufurate:


Ndipo Solomoni analamulira maiko onse, kuyambira ku Yufurate kufikira ku dziko la Afilisti ndi ku malire a Ejipito; anthu anabwera nayo mitulo namtumikira Solomoni masiku onse a moyo wake.


Pakuti analamulira dziko lonse lili tsidya lino la Yufurate, kuyambira ku Tifisa kufikira ku Gaza, inde mafumu onse a ku tsidya lino la Yufurate; nakhala ndi mtendere kozungulira konseko.


Ndipo Davide anakantha Hadadezere mfumu ya Zoba ku Hamati, pomuka iye kukhazikitsa ulamuliro wake ku mtsinje wa Yufurate.


Ndipo adzachita ufumu kuchokera kunyanja kufikira kunyanja, ndi kuchokera ku Mtsinje kufikira malekezero a dziko lapansi.


Ndipo ndidzalemba malire ako kuyambira ku Nyanja Yofiira, kufikira ku nyanja ya Afilisti, ndi kuyambira kuchipululu kufikira ku Nyanja; popeza ndidzapereka okhala m'dzikolo m'dzanja lako, ndipo uziwaingitsa pamaso pako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa