Masalimo 80:11 - Buku Lopatulika11 Unatambalitsa mphanda zake mpaka kunyanja, ndi mitsitsi yake kufikira ku Mtsinje. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Unatambalitsa mphanda zake mpaka kunyanja, ndi mitsitsi yake kufikira ku Mtsinje. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Nthambizo zidafika mpaka ku nyanja yaikulu yakuzambwe, ndipo mphukira zake mpaka ku mtsinje waukulu wakuvuma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Unatambalitsa nthambi zake mpaka ku nyanja, mphukira zake mpaka ku mtsinje. Onani mutuwo |