Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 80:10 - Buku Lopatulika

10 Mthunzi wake unaphimba mapiri, ndi nthambi zake zikunga mikungudza ya Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Mthunzi wake unaphimba mapiri, ndi nthambi zake zikunga mikungudza ya Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Mapiri adaphimbidwa ndi mthunzi wake, mikungudza yaikulu yomwe idaphimbidwa ndi nthambi zake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Mapiri anaphimbidwa ndi mthunzi wake, mikungudza yamphamvu ndi nthambi zake.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 80:10
2 Mawu Ofanana  

Mitengo ya Yehova yadzala ndi madzi; mikungudza ya ku Lebanoni imene anaioka;


Ndipo ndinatuma mavu atsogolere inu, amene anawaingitsa pamaso panu, ndiwo mafumu awiri a Aamori; osati ndi lupanga lako, kapena ndi uta wako ai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa