Masalimo 79:8 - Buku Lopatulika8 Musakumbukire motitsutsa mphulupulu za makolo athu; nsoni zokoma zanu zitipeze msanga, pakuti tafooka kwambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Musakumbukire motitsutsa mphulupulu za makolo athu; nsoni zokoma zanu zitipeze msanga, pakuti tafooka kwambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Musatilange ife chifukwa cha machimo a makolo athu. Mutichitire chifundo msanga, chifukwa tatsitsidwa kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Musatilange chifukwa cha machimo a makolo athu chifundo chanu chibwere msanga kukumana nafe, pakuti tili ndi chosowa chachikulu. Onani mutuwo |