Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 79:7 - Buku Lopatulika

7 Pakuti anathera Yakobo, napasula pokhalira iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Pakuti anathera Yakobo, napasula pokhalira iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Pakuti ameza anthu a Yakobe, ndipo dziko lao alisandutsa bwinja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 pakuti iwo ameza Yakobo ndi kuwononga dziko lawo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 79:7
9 Mawu Ofanana  

kuti akwaniridwe mau a Yehova pakamwa pa Yeremiya, mpaka dziko linakondwera nao masabata ake; masiku onse a kupasuka kwake linasunga Sabata, kukwaniritsa zaka makumi asanu ndi awiri.


Nguluwe zochokera kuthengo ziukumba, ndi nyama za kuchidikha ziudya.


Musakwiye kopambana, Yehova, musakumbukire zoipa nthawi zonse; taonani, yang'anani ife, tikupembedzani Inu, ife tonse tili anthu anu.


Aramu patsogolo ndi Afilisti pambuyo; ndipo iwo adzadya Israele ndi kukamwa koyasama. Mwa izi zonse mkwiyo wake sunachoke, koma dzanja lake lili chitambasulire.


Onse amene anazipeza anazidya; adani ao anati, Sitipalamula mlandu, chifukwa iwo anachimwira Yehova, ndiye mokhalamo zolungama, Yehova, chiyembekezo cha atate ao.


Ndipo ndikwiya nao amitundu okhala osatekeseka ndi mkwiyo waukulu; pakuti ndinakwiya pang'ono, ndipo anathandizira choipa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa