Masalimo 79:6 - Buku Lopatulika6 Thirirani mkwiyo wanu pa akunja osadziwa Inu, ndi pa maufumu osaitana pa dzina lanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Thirirani mkwiyo wanu pa akunja osadziwa Inu, ndi pa maufumu osaitana pa dzina lanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Gwetsani ukali wanu pa mitundu ya anthu osakudziŵani, ndiponso pa maufumu osatama dzina lanu mopemba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Khuthulirani ukali wanu pa anthu a mitundu ina amene sakudziwani Inu, pa maufumu amene sayitana pa dzina lanu; Onani mutuwo |