Masalimo 79:5 - Buku Lopatulika5 Yehova, mudzakwiya nthawi zonse kufikira liti? Nidzatentha nsanje yanu ngati moto? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Yehova, mudzakwiya nthawi zonse kufikira liti? Nidzatentha nsanje yanu ngati moto? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mpaka liti, Inu Chauta? Kodi mudzakhalabe wokwiya mpaka muyaya? Kodi nsanje yanu idzayakabe ngati moto? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mpaka liti Inu Yehova? Kodi mudzakwiya mpaka muyaya? Kodi mpaka liti nsanje yanu idzayaka ngati moto? Onani mutuwo |