Masalimo 79:4 - Buku Lopatulika4 Takhala chotonza cha anansi athu, ndi choseketsa ndi cholalatitsa iwo akutizinga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Takhala chotonza cha anansi athu, ndi choseketsa ndi cholalatitsa iwo akutizinga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ife tasanduka chinthu chonyozeka kwa anzathu, anthu a mitundu ina amatinyodola ndi kutiseka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ife ndife chinthu chonyozeka kwa anansi athu, choseketsa ndi cholalatiridwa kwa iwo amene atizungulira. Onani mutuwo |
Pakuti atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele: Monga mkwiyo wanga ndi ukali wanga wathiridwa kwa okhala mu Yerusalemu, momwemo ukali wanga udzathiridwa pa inu, pamene mudzalowa mu Ejipito; ndipo mudzakhala chitukwano, ndi chizizwitso, ndi chitemberero, ndi chitonzo; ndipo simudzaonananso malo ano.