Masalimo 79:3 - Buku Lopatulika3 Anakhetsa mwazi wao ngati madzi pozungulira Yerusalemu; ndipo panalibe wakuwaika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Anakhetsa mwazi wao ngati madzi pozungulira Yerusalemu; ndipo panalibe wakuwaika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Akhetsa magazi ao ngati madzi, ponse pozungulira Yerusalemu, ndipo palibe woti nkuika maliro ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Akhetsa magazi monga madzi kuzungulira Yerusalemu yense, ndipo palibe wina woti ayike mʼmanda anthu akufa. Onani mutuwo |