Masalimo 79:2 - Buku Lopatulika2 Anapereka mitembo ya atumiki anu ikhale chakudya cha mbalame za mlengalenga, nyama ya okondedwa anu anaipereka kwa zilombo za m'dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Anapereka mitembo ya atumiki anu ikhale chakudya cha mbalame za mlengalenga, nyama ya okondedwa anu anaipereka kwa zilombo za m'dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ataya mitembo ya atumiki anu kwa mbalame zamumlengalenga, kuti ikhale chakudya chake, ataya matupi a anthu anu oyera mtima kwa zilombo zakuthengo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iwo anapereka mitembo ya atumiki anu kwa mbalame zamlengalenga ngati chakudya, matupi a oyera mtima anu kwa zirombo za dziko lapansi. Onani mutuwo |