Masalimo 79:1 - Buku Lopatulika1 Mulungu, akunja alowa m'cholowa chanu; anaipsa Kachisi wanu woyera; anachititsa Yerusalemu bwinja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mulungu, akunja alowa m'cholandira chanu; anaipsa Kachisi wanu woyera; anachititsa Yerusalemu bwinja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu Mulungu, anthu akunja aloŵerera m'dziko la anthu anu, aipitsa Nyumba yanu yoyera. Asandutsa Yerusalemu bwinja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Inu Mulungu, anthu a mitundu ina alowerera mʼcholowa chanu; ayipitsa Nyumba yanu yoyera, asandutsa Yerusalemu kukhala bwinja. Onani mutuwo |