Masalimo 78:72 - Buku Lopatulika72 Potero anawaweta monga mwa mtima wake wangwiro; nawatsogolera ndi luso la manja ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201472 Potero anawaweta monga mwa mtima wake wangwiro; nawatsogolera ndi luso la manja ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa72 Davide adaŵasamala ndi mtima wolungama, naŵatsogolera ndi dzanja lake mwaluso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero72 Ndipo Davide anawaweta ndi mtima wolungama; ndi manja aluso anawatsogolera. Onani mutuwo |