Masalimo 78:71 - Buku Lopatulika71 Anamtenga kuja anatsata zoyamwitsa, awete Yakobo, anthu ake, ndi Israele, cholowa chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201471 Anamtenga kuja anatsata zoyamwitsa, awete Yakobo, anthu ake, ndi Israele, cholandira chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa71 Adamtenga kumene ankaŵeta nkhosa zimene zinali ndi ana, kuti adzakhale mbusa wa Yakobe, fuko lake, wa Israele, choloŵa chake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero71 kuchokera koyangʼanira nkhosa anamubweretsa kuti akhale mʼbusa wa anthu ake, Yakobo, wa Israeli cholowa chake. Onani mutuwo |