Masalimo 78:53 - Buku Lopatulika53 Ndipo anawatsogolera mokhulupirika, kotero kuti sanaope; koma nyanja inamiza adani ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201453 Ndipo anawatsogolera mokhulupirika, kotero kuti sanaope; koma nyanja inamiza adani ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa53 Adaŵatsogolera bwino lomwe kotero kuti sanalikuwopa, koma nyanja idamiza adani ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero53 Anawatsogolera bwinobwino kotero kuti analibe mantha koma nyanja inamiza adani awo. Onani mutuwo |