Masalimo 78:54 - Buku Lopatulika54 Ndipo anawafikitsa kumalire a malo ake oyera, kuphiri ili, dzanja lamanja lake lidaligula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201454 Ndipo anawafikitsa kumalire a malo ake oyera, kuphiri ili, dzanja lamanja lake lidaligula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa54 Adaŵafikitsa ku dziko lake loyera, ku dziko lamapiri limene adaŵagonjetsera ndi dzanja lake lamphamvu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero54 Kotero anawafikitsa ku malire a dziko lake loyera, ku dziko lamapiri limene dzanja lake lamanja linawatengera. Onani mutuwo |