Masalimo 78:52 - Buku Lopatulika52 Koma anatulutsa anthu ake ngati nkhosa, nawatsogoza ngati gulu la zoweta m'chipululu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201452 Koma anatulutsa anthu ake ngati nkhosa, nawatsogoza ngati gulu la zoweta m'chipululu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa52 Tsono Mulungu adaŵatulutsa anthu ake ngati nkhosa, naŵatsogolera m'chipululu ngati zoŵeta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero52 Koma Iye anatulutsa anthu ake ngati ziweto; anawatsogolera ngati nkhosa kudutsa mʼchipululu. Onani mutuwo |