Masalimo 78:5 - Buku Lopatulika5 Anakhazika mboni mwa Yakobo, naika chilamulo mwa Israele, ndizo analamulira atate athu, akazidziwitse ana ao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Anakhazika mboni mwa Yakobo, naika chilamulo mwa Israele, ndizo analamulira atate athu, akazidziwitse ana ao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Adapereka mau odzichitira umboni kwa Yakobe, adakhazikitsa malamulo ake mu Israele. Adalamula makolo athu kuti aziŵaphunzitsa ana ao malamulowo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Iye anapereka mawu wodzichitira umboni kwa Yakobo ndi kukhazikitsa lamulo mu Israeli, zimene analamulira makolo athu kuphunzitsa ana awo, Onani mutuwo |