Masalimo 78:23 - Buku Lopatulika23 Koma analamulira mitambo ili m'mwamba, natsegula m'makomo a kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Koma analamulira mitambo ili m'mwamba, natsegula m'makomo a kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Komabe Iye adalamula mitambo yamumlengalenga, natsekula zitseko zakumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Komabe Iye anapereka lamulo kwa mitambo mmwamba ndi kutsekula makomo a mayiko akumwamba; Onani mutuwo |