Masalimo 78:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo anawavumbitsira mana, adye, nawapatsa tirigu wa kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo anawavumbitsira mana, adye, nawapatsa tirigu wa kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Poŵagwetsera mana kuti adye, adaŵapatsa tirigu wakumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 anagwetsa mana kuti anthu adye, anawapatsa tirigu wakumwamba. Onani mutuwo |