Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 78:2 - Buku Lopatulika

2 Ndidzatsegula pakamwa panga mofanizira; ndidzatchula zinsinsi zoyambira kale.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndidzatsegula pakamwa panga mofanizira; ndidzatchula zinsinsi zoyambira kale.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Ndidzakusimbirani fanizo. Ndidzalankhula nkhani zobisika zakalekale,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Ndidzatsekula pakamwa panga mʼmafanizo, ndidzayankhula zinthu zobisika, zinthu zakalekale

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 78:2
8 Mawu Ofanana  

Ndidzatchera khutu kufanizo, ndidzafotokozera chophiphiritsa changa poimbira.


Ndidzaoperanji masiku oipa, pondizinga amphulupulu onditsata kuchidendene?


kuzindikira mwambi ndi tanthauzo lake, mau a anzeru, ndi zophiphiritsa zao.


Kumbukirani zinthu zoyamba zakale, kuti Ine ndine Mulungu, ndipo palibenso wina; Ine ndine Mulungu, ndipo palibenso wina wofanana ndi Ine;


ndipo sanalankhule nao wopanda fanizo: koma m'tseri anatanthauzira zonse kwa ophunzira ake.


Ndipo Yehova anawazula m'nthaka mwao mokwiya ndi mozaza, ndi mu ukali waukulu, nawaponya m'dziko lina, monga lero lino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa