Masalimo 77:9 - Buku Lopatulika9 Kodi Mulungu waiwala kuchita chifundo? Watsekereza kodi nsoni zokoma zake mumkwiyo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Kodi Mulungu waiwala kuchita chifundo? Watsekereza kodi nsoni zokoma zake mumkwiyo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Kodi Mulungu waiŵala kukoma mtima kwake kuja? Kodi wakwiya ndi kuleka chifundo chake chija?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Kodi Mulungu wayiwala kukhala wokoma mtima? Kodi mu mkwiyo wake waleka chifundo chake?” Onani mutuwo |