Masalimo 77:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo ndinati, Chindiwawa ichi; koma ndikumbukira zaka za dzanja lamanja la Wam'mwambamwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo ndinati, Chindilaka ichi; koma ndikumbukira zaka za dzanja lamanja la Wam'mwambamwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Chondiŵaŵa ndi chakuti, Mulungu Wopambanazonse wasintha mchitidwe wake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndipo ndinaganiza, “Pa izi ine ndidzapemphanso: zaka za dzanja lamanja la Wammwambamwamba. Onani mutuwo |