Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 74:5 - Buku Lopatulika

5 Anaoneka ngati osamula nkhwangwa kunkhalango.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Anaoneka ngati osamula nkhwangwa kunkhalango.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Adadulamo zonse, monga momwe anthu amadulira mitengo m'nkhalango.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Iwo anachita ngati anthu oti anyamula mbendera zawo kuti adule mitengo mʼnkhalango.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 74:5
3 Mawu Ofanana  

Ndipo tsono, lamulirani kuti anditemere mitengo yamkungudza ku Lebanoni, ndipo akapolo anga adzakhala ndi akapolo anu, ndipo ndidzakupatsani mphotho ya akapolo anu monga mudzanena; popeza mudziwa kuti pakati pa ife palibe mmisiri wakudziwa kutema mitengo ngati anthu a ku Sidoni.


ndiye mwana wa munthu wamkazi wa ana aakazi a Dani, ndipo atate wake ndiye munthu wa ku Tiro, wodziwa kuchita ndi golide, ndi siliva, ndi mkuwa, ndi chitsulo, ndi mwala, ndi mitengo, ndi thonje lofiirira, ndi lamadzi, ndi bafuta la thonje losansitsa ndi lofiira, ndi kuzokota mazokotedwe ali onse, ndi kulingirira chopanga chilichonse; kuti ampatse pokhala pamodzi ndi aluso anu, ndi aluso a mbuye wanga Davide atate wanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa