Masalimo 74:4 - Buku Lopatulika4 Otsutsana ndi Inu abangula pakati pa msonkhano wanu; aika mbendera zao zikhale zizindikiro. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Otsutsana ndi Inu abangula pakati pa msonkhano wanu; aika mbendera zao zikhale zizindikiro. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adani anu abangula m'malo anu opatulika, adaikamo mbendera zao kusonyeza kuti agonjetsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Adani anu anabangula pa malo pamene Inu munkakumana nafe; anayimika mbendera zawo monga zizindikiro zachigonjetso. Onani mutuwo |