Masalimo 74:23 - Buku Lopatulika23 Musaiwale mau a iwo otsutsana ndi Inu; kusokosera kwa iwo akuukirani Inu kumakwera kosaleka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Musaiwale mau a iwo otsutsana ndi Inu; kusokosera kwa iwo akuukirani Inu kumakwera kosaleka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Musalekerere chiwawa cha amaliwongo anu, phokoso la adani anu limene likungokulirakulira nthaŵi zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Musalekerere phokoso la otsutsana nanu, chiwawa cha adani anu, chimene chikumveka kosalekeza. Onani mutuwo |