Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 74:22 - Buku Lopatulika

22 Nyamukani, Mulungu, mudzinenere mlandu nokha; kumbukirani momwe akutonzani wopusa tsiku lonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Nyamukani, Mulungu, mudzinenere mlandu nokha; kumbukirani momwe akutonzani wopusa tsiku lonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Dzambatukani, Inu Mulungu, tiyeni mudziteteze pa mlandu wanuwo, kumbukirani kuti anthu amwano amakunyodolani tsiku lonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Dzukani Inu Mulungu ndipo dzitetezeni pa mlandu; kumbukirani momwe opusa akukunyozerani tsiku lonse.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 74:22
9 Mawu Ofanana  

Tcherani khutu lanu, Yehova nimumve; tsegulani maso anu, Yehova, nimupenye; ndipo imvani mau a Senakeribu, amene anatumiza kutonza nao Mulungu wamoyo.


Galamukani, ndipo khalani maso kundiweruzira mlandu wanga, Mulungu wanga ndi Ambuye wanga.


Chitsiru chimati mumtima mwake, Kulibe Mulungu. Achita zovunda, achita chosalungama chonyansa; kulibe wakuchita bwino.


Mukumbukire ichi, Yehova, mdaniyo anatonza, ndipo anthu opusa ananyoza dzina lanu.


Chifukwa chake kodi ndichitenji pano? Ati Yehova; popeza anthu anga achotsedwa popanda kanthu? Akuwalamulira awaliritsa, ati Yehova; ndipo dzina langa lichitidwa mwano tsiku lonse kosalekeza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa