Masalimo 75:1 - Buku Lopatulika1 Tikuyamikani Inu, Mulungu; tiyamika, pakuti dzina lanu lili pafupi; afotokozera zodabwitsa zanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Tikuyamikani Inu, Mulungu; tiyamika, pakuti dzina lanu lili pafupi; afotokozera zodabwitsa zanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tikukuthokozani Inu Mulungu, ndithu tikukuthokozani. Tikutchula dzina lanu mopemphera ndipo tikulalika ntchito zanu zodabwitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tikuthokoza Inu Mulungu, tikuthokoza, pakuti dzina lanu lili pafupi nafe, anthutu amafotokoza za ntchito zanu zodabwitsa. Onani mutuwo |