Masalimo 74:14 - Buku Lopatulika14 Mudaphwanya mitu ya Leviyatani; mudampereka akhale chakudya cha zilombo za m'chipululu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Mudaphwanya mitu ya Leviyatani; mudampereka akhale chakudya cha zilombo za m'chipululu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Mudatswanya mitu ya Leviyatani, chilombo cham'madzi chija, nkuitaya kuti ikhale chakudya cha zilombo zam'chipululu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndinu amene munaphwanya mitu ya Leviyatani ndi kuyipereka ngati chakudya cha zirombo za mʼchipululu. Onani mutuwo |