Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 74:11 - Buku Lopatulika

11 Mubwezeranji dzanja lanu, ndilo dzanja lamanja lanu? Mulitulutse kuchifuwa chanu ndipo muwatheretu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Mubwezeranji dzanja lanu, ndilo dzanja lamanja lanu? Mulitulutse kuchifuwa chanu ndipo muwatheretu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Chifukwa chiyani mukubisa dzanja lanu lotithandiza? Bwanji dzanja lanu lamanja likungokhala pachifuwa panu?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Chifukwa chiyani mukubweza dzanja lanu lamanja? Litulutseni kuchoka pachifuwa chanu ndipo muwawononge!

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 74:11
5 Mawu Ofanana  

Galamukani, mugoneranji, Ambuye? Ukani, musatitaye chitayire.


Kodi mudzadziletsa pa zinthuzi, Yehova? Kodi Inu mudzakhala chete ndi kutivutitsa ife zolimba?


Pokwiya moopsa walikha nyanga zonse za Israele; wabweza m'mbuyo dzanja lake lamanja pamaso pa adaniwo, natentha Yakobo ngati moto wamalawi wonyambita mozungulira.


Ndipo pamene anthu anafika ku zithandozo, akulu a Israele anati, Yehova anatikanthiranji lero pamaso pa Afilisti? Tikadzitengere likasa la chipangano la Yehova ku Silo, kuti likabwera pakati pa ife, lidzatipulumutsa m'dzanja la adani athu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa