Masalimo 74:10 - Buku Lopatulika10 Wotsutsanayo adzatonza kufikira liti, Mulungu? Kodi mdani adzanyoza dzina lanu nthawi yonse? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Wotsutsanayo adzatonza kufikira liti, Mulungu? Kodi mdani adzanyoza dzina lanu nthawi yonse? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Inu Mulungu, adani athuŵa adzanyodolabe mpaka liti? Amaliwongowo adzanyozabe dzina lanu mpaka muyaya? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kodi mpaka liti, mdani adzanyoze Inu Mulungu? Kodi amaliwongowa adzapeputsa dzina lanu kwamuyaya? Onani mutuwo |