Masalimo 73:8 - Buku Lopatulika8 Achita zaphwete nalankhula moipa za kusautsa, alankhula modzitama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Achita zaphwete nalankhula moipa za kusautsa, alankhula modzitama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Amanyodola ndi kumalankhula zoipa, amadzikuza ndi kumaopseza ena kuti, “Tikupsinjani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Iwowo amanyogodola ndi kumayankhula zoyipa; mwa kudzikuza kwawo amaopseza ena nʼkumati, “Tikuponderezani.” Onani mutuwo |