Masalimo 73:7 - Buku Lopatulika7 Kunenepa kwao kutuzulitsa maso ao, malingaliro a mitima yao asefukira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Kunenepa kwao kutuzulitsa maso ao, malingaliro a mitima yao asefukira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Maso ao ndi otupa ndi kunenepa. Mitima yao ndi yodzaza ndi maganizo ofuna kuchita zoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Mʼmitima yawo yokhota mumachokera zolakwa; zoyipa zochokera mʼmaganizo awo sizidziwa malire. Onani mutuwo |