Masalimo 73:4 - Buku Lopatulika4 Pakuti palibe zomangira pakufa iwo, ndi mphamvu yao njolimba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pakuti palibe zomangira pakufa iwo, ndi mphamvu yao njolimba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Iwowo samva kupweteka konse. Matupi ao ndi onenepa ndi athanzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iwo alibe zosautsa; matupi awo ndi athanzi ndi amphamvu. Onani mutuwo |